Malawi Native Anthem Text
National Anthem
1.
Mlungu dalitsani Malawi,
Mumsunge m'mtendere.
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje.
Lunzitsani mitima yathu,
Kuti tisaope.
Mdalitse Mtsogo leri na fe,
Ndi Mai Malawi.
2.
Malawi ndziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,
Ndithudi tadala.
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
N'mphatso zaulere.
Nkhalango, madambo abwino.
Ngwokoma Malawi.
3.
O! Ufulu tigwirizane,
Kukweza Malawi.
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire.
Pa nkhondo nkana pa mtendere,
Cholinga 'chimodzi.
Mai, bambo, tidzipereke,
Pokweza Malawi.
Sent by Carlos Andrй Pereira da Silva Branco
Share
More from National Anthem
Bangladesh Anthem Text
National Anthem
Albania Anthem Native Text
National Anthem
A Soldiers Song
National Anthem
Uganda Anthem
National Anthem
The Star-Spangled Banner (USA Anthem)
National Anthem
Spain National Anthem - Proposed January 2008
National Anthem
Colombia Native Anthem Text
National Anthem
Fratelli D'Italia
National Anthem
La Borique\u00f1a
National Anthem
China National Anthem
National Anthem
Russian Federation National Anthem
National Anthem
French Canadian Anthem Text
National Anthem
Germany Anthem
National Anthem
United Kingdom Anthem Text
National Anthem
Mexican National Anthem
National Anthem
Jana Gana Mana
National Anthem
O Canada (Canadian National Anthem)
National Anthem
El Salvador
National Anthem
Zambia Anthem Text
National Anthem
Indonesian National Anthem
National Anthem